Pular para o conteúdo
Publicidade

GENESIS 40

6 Mmawa wake, Yosefe atabwera, anaona kuti nkhope zawo zinali zakugwa. 7 Choncho anafunsa akuluakulu a kwa Farao amene anali naye mʼndende muja kuti, "Bwanji nkhope zanu zili zachisoni lero?"

Veja também