3 "Rubeni, ndiwe woyamba kubadwa;
mphamvu yanga ndiponso chizindikiro choyamba cha mphamvu zanga,
wopambana pa ulemerero ndi mphamvu.
4 Wokokoma ngati madzi a chigumula, koma sudzakhalanso wopambana,
iwe unagona pa bedi la abambo ako,
ndithu unayipitsa bedi la mdzakazi wake.