Chenjezo pa Kusakhulupirira
7 Tsono monga Mzimu Woyera akuti,
"Lero mukamva mawu ake,
8 musawumitse mitima yanu
ngati munachitira pamene munawukira,
pa nthawi yoyesedwa mʼchipululu.
7 Tsono monga Mzimu Woyera akuti,
"Lero mukamva mawu ake,
8 musawumitse mitima yanu
ngati munachitira pamene munawukira,
pa nthawi yoyesedwa mʼchipululu.