19 Ambuye Yehova ndiye mphamvu yanga;
amalimbitsa miyendo yanga ngati ya mbawala yayikazi,
amandithandiza kukafika pamwamba pa phiri.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za nsambo.
19 Ambuye Yehova ndiye mphamvu yanga;
amalimbitsa miyendo yanga ngati ya mbawala yayikazi,
amandithandiza kukafika pamwamba pa phiri.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za nsambo.