Pular para o conteúdo
Publicidade

Joel 2

Ngʼambani Mtima Wanu

12 "Ngakhale tsopano,

bwererani kwa Ine ndi mtima wanu wonse

posala zakudya ndi kukhetsa misozi," akutero Yehova.

13 Ngʼambani mtima wanu

osati zovala zanu.

Bwererani kwa Yehova Mulungu wanu,

pakuti Iye ndi wokoma mtima ndi wachifundo,

wosakwiya msanga ndi wachikondi chochuluka,

ndipo amaleka kubweretsa mavuto.

Veja também

Joel
Ver todos os capítulos de Joel