Pular para o conteúdo
Publicidade

João 1

Yesu Mwana Wankhosa wa Mulungu

29 Pa tsiku lotsatira Yohane anaona Yesu akubwera kwa iye ndipo anati, "Taonani, Mwana Wankhosa wa Mulungu, amene achotsa tchimo la dziko lapansi!

34 Ine ndaona ndipo ndikuchitira umboni kuti uyu ndi Mwana wa Mulungu."

Veja também