Pular para o conteúdo
Publicidade

João 1

9 Kuwunika koona kumene kuwunikira munthu aliyense kunabwera ku dziko lapansi.

10 Iye anali mʼdziko lapansi, ndipo ngakhale kuti dziko lapansi linalengedwa ndi Iye, dziko lapansilo silinamuzindikire Iye.

Veja também