33 Yesu ataona iye akulira, ndi Ayuda amene anabwera naye akuliranso, anakhudzidwa kwambiri ndi kuvutika mu mzimu. 34 Iye anafunsa kuti, "Kodi mwamuyika kuti?"
Iwo anayankha kuti, "Ambuye tiyeni mukaone."
35 Yesu analira.
33 Yesu ataona iye akulira, ndi Ayuda amene anabwera naye akuliranso, anakhudzidwa kwambiri ndi kuvutika mu mzimu. 34 Iye anafunsa kuti, "Kodi mwamuyika kuti?"
Iwo anayankha kuti, "Ambuye tiyeni mukaone."
35 Yesu analira.