Yesu Alowa mu Yerusalemu
12 Tsiku lotsatira, gulu lalikulu la anthu lomwe linabwera kuphwando linamva kuti Yesu anali mʼnjira kupita ku Yerusalemu. 13 Iwo anatenga nthambi za kanjedza ndi kupita kukakumana naye, akufuwula kuti,
"Hosana!
"Wodala Iye amene akubwera mʼdzina la Ambuye!
"Yodala Mfumu ya Israeli!"