Pular para o conteúdo
Publicidade

João 13

12 Iye atamaliza kusambitsa mapazi awo anavala zovala zake ndi kubwerera pamalo pake. Iye anawafunsa kuti, "Kodi mukuzindikira zimene ndakuchitirani inu? 15 Ine ndakupatsani chitsanzo kuti muzichita monga Ine ndachitira.

Veja também