Pular para o conteúdo
Publicidade

YOHANE 20

14 Atanena izi, iye anatembenuka ndipo anaona Yesu atayima potero koma iye sanazindikire kuti anali Yesu.

15 Iye anati, "Amayi, mukulira chifukwa chiyani? Ndani amene mukumufunafuna?"

Poganiza kuti anali mwini munda, iye anati, "Bwana, ngati inu mwamuchotsa, ndiwuzeni kumene mwamuyika, ndipo ine ndikamutenga."

16 Yesu anati kwa iye, "Mariya."

Anatembenukira kwa Iye nafuwula mu Chiaramaiki kuti, "Raboni!" (kutanthauza Mphunzitsi).

Veja também