Yesu Abwezeretsa Petro
15 Iwo atamaliza kudya chakudya chammawa, Yesu anati kwa Simoni Petro, "Simoni, mwana wa Yohane, kodi umandikonda Ine kuposa mmene amandikondera awa?"
Iye anati, "Inde Ambuye, Inu mukudziwa kuti Ine ndimakukondani."
Yesu anati, "Samala ana ankhosa anga."