Pular para o conteúdo
Publicidade

João 21

17 Yesu anati kwa iye kachitatu, "Simoni, mwana wa Yohane, kodi umandikondadi Ine?"

Petro anadzimvera chisoni chifukwa Yesu anamufunsa kachitatu kuti, "Kodi umandikonda Ine?" Iye anati, "Ambuye, Inu mudziwa zinthu zonse. Inu mukudziwa kuti Ine ndimakukondani."

Yesu anati, "Dyetsa nkhosa zanga.

Veja também