Pular para o conteúdo
Publicidade

João 7

3 abale a Yesu anati kwa Iye, "Inu muyenera kuchoka kuno ndi kupita ku Yudeya, kuti ophunzira anu akaone zodabwitsa zomwe mumachita. 4 Palibe wina aliyense amene amafuna kukhala wodziwika amachita zinthu mseri. Popeza Inu mukuchita zinthu izi, mudzionetsere nokha ku dziko la pansi." 5 Pakuti ngakhale abale ake omwe sanamukhulupirire.

Veja também