Pular para o conteúdo
Publicidade

Juízes 14

3 Koma abambo ndi amayi ake anayankha kuti, "Kodi palibe mkazi pakati pa abale akowa kapena pakati pa anthu a mtundu wako, kuti iwe upite kukapeza mkazi kwa Afilisti anthu osachita mdulidwe?"

Koma Samsoni anawuza abambo ake kuti, "Kanditengereni ameneyu basi, pakuti ndamukonda."

Veja também