Publicidade

Lucas 1

Nyimbo ya Mariya

46 Ndipo Mariya anati:

"Moyo wanga ulemekeza Ambuye.

47 Ndipo mzimu wanga ukondwera mwa Mulungu Mpulumutsi wanga,

48 pakuti wakumbukira

kudzichepetsa kwa mtumiki wake.

Kuyambira tsopano mibado yonse idzanditcha wodala,

49 pakuti Wamkuluyo wandichitira ine zinthu zazikulu,

dzina lake ndi loyera.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-