Publicidade

Lucas 11

2 Yesu anawawuza kuti, "Pamene mukupemphera muzinena kuti:

" Atate,

dzina lanu lilemekezedwe,

ufumu wanu ubwere.

3 Mutipatse chakudya chathu chalero,

4 mutikhululukire machimo athu,

monga ifenso timakhululukira aliyense amene watilakwira.

Ndipo musalole kuti tigwe mʼmayesero.’ "

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-