Pular para o conteúdo
Publicidade

Lucas 19

37 Iye atafika pafupi ndi pamene msewu umatsikira ku phiri la Olivi, gulu lonse la ophunzira linayamba kuyamika Mulungu mwachimwemwe ndi mawu ofuwula chifukwa cha zodabwitsa zonse anaziona.

38 "Yodala mfumu imene ikubwera mʼdzina la Ambuye!"

"Mtendere kumwamba ndi ulemerero mmwambamwamba!"

Veja também