35 Kenaka Yesu anawafunsa iwo kuti, "Ine nditakutumizani wopanda chikwama cha ndalama, thumba kapena nsapato, kodi inu munasowa kanthu?"
Iwo anayankha kuti, "Palibe chimene tinasowa."
35 Kenaka Yesu anawafunsa iwo kuti, "Ine nditakutumizani wopanda chikwama cha ndalama, thumba kapena nsapato, kodi inu munasowa kanthu?"
Iwo anayankha kuti, "Palibe chimene tinasowa."