Pular para o conteúdo
Publicidade

Lucas 22

Amugwira Yesu

47 Pamene Iye ankayankhulabe, gulu la anthu linabwera, ndipo munthu wotchedwa Yudasi, mmodzi wa khumi ndi awiriwo analitsogolera. Iye anamuyandikira Yesu kuti amupsompsone. 48 Koma Yesu anamufunsa kuti, "Yudasi, kodi ukupereka Mwana wa Munthu ndi mpsopsono?"

Veja também