10 Gulu la anthuwo linafunsa kuti, "Nanga tsono tichite chiyani?"
11 Yohane anayankha kuti, "Munthu amene ali ndi malaya awiri apatseko amene alibe, ndi amene ali ndi chakudya achitenso chimodzimodzi."
10 Gulu la anthuwo linafunsa kuti, "Nanga tsono tichite chiyani?"
11 Yohane anayankha kuti, "Munthu amene ali ndi malaya awiri apatseko amene alibe, ndi amene ali ndi chakudya achitenso chimodzimodzi."