Pular para o conteúdo
Publicidade

Lucas 4

18 "Mzimu wa Ambuye ali pa Ine;

chifukwa wandidzoza

kuti ndilalikire Uthenga Wabwino kwa osauka.

Wandituma kuti ndilalikire kwa a mʼndende kuti amasulidwe

ndi kwa osaona kuti apenyenso,

kumasulidwa kwa osautsidwa,

19 ndi kulalikira za nthawi imene Ambuye adzakomere mtima anthu awo."

Veja também