3 Mdierekezi anati kwa Iye, "Ngati ndiwe Mwana wa Mulungu, uza mwala uwu kuti usanduke buledi."
4 Yesu anayankha kuti, "Zalembedwa: ‘Munthu sadzakhala ndi moyo ndi chakudya chokha.’ "
3 Mdierekezi anati kwa Iye, "Ngati ndiwe Mwana wa Mulungu, uza mwala uwu kuti usanduke buledi."
4 Yesu anayankha kuti, "Zalembedwa: ‘Munthu sadzakhala ndi moyo ndi chakudya chokha.’ "