Pular para o conteúdo
Publicidade

Lucas 5

Yesu Afunsidwa za Kusala Kudya

33 Iwo anati kwa Iye, "Ophunzira a Yohane amasala kudya ndi kupemphera kawirikawiri, monganso ophunzira a Afarisi, koma anu amangodya ndi kumwa."

34 Yesu anawayankha kuti, "Kodi alendo a mkwati angasale kudya pamene mkwati ali pakati pawo? 35 Koma nthawi ikubwera pamene mkwati adzachotsedwa pakati pawo. Masiku amenewo adzasala kudya."

Veja também