Pular para o conteúdo
Publicidade

LUKA 7

33 Pakuti Yohane Mʼbatizi sanabwere kudzadya buledi kapena kumwa vinyo, koma inu mumati, Ali ndi chiwanda. 34 Mwana wa Munthu anabwera nadya ndi kumwa, ndipo inu mukuti, Ali ndi dyera komanso ndi woledzera, bwenzi la amisonkho ndi ochimwa.

Veja também