Publicidade

Lamentações 3

31 Chifukwa Ambuye satayiratu

anthu nthawi zonse.

32 Ngakhale amabweretsa zowawa, Iye adzawachitira chifundo,

chifukwa chikondi chake ndi chosatha.

33 Pakuti sabweretsa masautso mwadala,

kapena zowawa kwa ana a anthu.

Veja também

Publicidade
Lamentações
Ver todos os capítulos de Lamentações
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-22_10-02-25-