31 Chifukwa Ambuye satayiratu
anthu nthawi zonse.
32 Ngakhale amabweretsa zowawa, Iye adzawachitira chifundo,
chifukwa chikondi chake ndi chosatha.
33 Pakuti sabweretsa masautso mwadala,
kapena zowawa kwa ana a anthu.
31 Chifukwa Ambuye satayiratu
anthu nthawi zonse.
32 Ngakhale amabweretsa zowawa, Iye adzawachitira chifundo,
chifukwa chikondi chake ndi chosatha.
33 Pakuti sabweretsa masautso mwadala,
kapena zowawa kwa ana a anthu.