Pular para o conteúdo
Publicidade

MALIRO 3

31 Chifukwa Ambuye satayiratu

anthu nthawi zonse.

32 Ngakhale amabweretsa zowawa, Iye adzawachitira chifundo,

chifukwa chikondi chake ndi chosatha.

33 Pakuti sabweretsa masautso mwadala,

kapena zowawa kwa ana a anthu.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também

Lamentações
Ver todos os capítulos de Lamentações