Publicidade

Marcos 15

Imfa ya Yesu

33 Pa ora lachisanu ndi chimodzi masana mdima unabwera pa dziko lonse mpaka pa ora lachisanu ndi chinayi masana. 34 Pa ora lachisanu ndi chinayi Yesu analira mofuwula kuti, "Eloi, Eloi, lama sabakitani?" Kutanthauza kuti, "Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji Ine?"

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-