Imfa ya Yesu
33 Pa ora lachisanu ndi chimodzi masana mdima unabwera pa dziko lonse mpaka pa ora lachisanu ndi chinayi masana. 34 Pa ora lachisanu ndi chinayi Yesu analira mofuwula kuti, "Eloi, Eloi, lama sabakitani?" Kutanthauza kuti, "Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji Ine?"