Pular para o conteúdo
Publicidade

Marcos 6

17 Pakuti Herode iye mwini analamula kuti amumange Yohane ndi kumuyika mʼndende. Anachita izi chifukwa cha Herodia, mkazi wa mʼbale wake Filipo, amene iye anamukwatira. 18 Pakuti Yohane ankanena kwa Herode kuti, "Sikololedwa kwa inu kuti mukwatire mkazi wa mʼbale wanu."

Veja também