Pular para o conteúdo
Publicidade

Marcos 9

28 Yesu atalowa mʼnyumba, ophunzira ake anamufunsa ali pa okha kuti, "Kodi ndi chifukwa chiyani ife sitinathe kutulutsa chiwandacho?"

29 Iye anayankha kuti, "Mtundu uwu umatuluka pokhapokha mwapemphera ndi kusala kudya."

Veja também