Pular para o conteúdo
Publicidade

Mateus 15

3 Yesu anayankha kuti, "Nanga chifukwa chiyani inu mumaphwanya lamulo la Mulungu chifukwa cha mwambo wa makolo anu? 4 Pakuti Mulungu anati, Lemekeza abambo ako ndi amayi akondipo aliyense amene atemberera abambo ake kapena amayi ake ayenera kuphedwa.

Veja também