Publicidade

Mateus 19

4 Iye anayankha kuti, "Kodi simunawerenge kuti pachiyambi Mulungu analenga iwo, mwamuna ndi mkazi? 5 Ndipo anati, Pa chifukwa ichi mwamuna adzasiya abambo ake ndi amayi ake nakaphatikana ndi mkazi wake, ndipo awiriwo adzakhala thupi limodzi. 6 Motero salinso awiri ayi koma mmodzi. Nʼchifukwa chake chimene Mulungu wachimanga pamodzi munthu wina asachilekanitse."

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-28_14-13-17-