Pular para o conteúdo
Publicidade

MATEYU 23

8 "Koma inu simuyenera kutchulidwa Aphunzitsi,popeza muli naye Mbuye mmodzi ndipo inu nonse ndinu abale. 9 Ndipo musamatchule wina aliyense pansi pano kuti Atate,pakuti muli ndi Atate mmodzi, ndipo ali kumwamba.

Veja também