Pular para o conteúdo
Publicidade

Mateus 24

23 Pa nthawi imeneyo ngati wina adzati kwa inu, Onani, Khristu ali pano!Kapena, Uyo ali ukoyo!Musakhulupirire. 24 Chifukwa akhristu onama ndi aneneri onama adzaoneka ndipo adzachita zizindikiro zazikulu ndi zodabwitsa kuti akanyenge ngakhale osankhidwawo ngati kukanakhala kotheka kutero. 25 Onani, ndakuwuzani izi nthawi isanafike.

Veja também