Publicidade

Mateus 5

3 "Odala ndi amene ali osauka mu mzimu,

chifukwa ufumu wakumwamba ndi wawo.

4 Odala ndi amene ali achisoni,

chifukwa adzatonthozedwa.

5 Odala ndi amene ali ofatsa,

chifukwa adzalandira dziko lapansi.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-28_14-13-17-