Pular para o conteúdo
Publicidade

MATEYU 5

3 "Odala ndi amene ali osauka mu mzimu,

chifukwa ufumu wakumwamba ndi wawo.

4 Odala ndi amene ali achisoni,

chifukwa adzatonthozedwa.

5 Odala ndi amene ali ofatsa,

chifukwa adzalandira dziko lapansi.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também