Pular para o conteúdo
Publicidade

Mateus 5

44 Koma Ine ndikuwuzani kuti, Kondani adani anu ndi kuwapempherera okuzunzani 45 kuti mukhale ana a Atate anu akumwamba, amene awalitsa dzuwa lake pa oyipa ndi pa abwino, nagwetsa mvula pa olungama ndi pa osalungama.

Veja também