Pular para o conteúdo
Publicidade

MATEYU 8

Yesu Achiritsa Anthu Ambiri

14 Ndipo Yesu atalowa mʼnyumba ya Petro, anaona mpongozi wake wa Petro ali gone akudwala malungo. 15 Ndipo Yesu anakhudza dzanja lake ndipo pomwepo anachira nayamba kumutumikira.

Veja também