Pular para o conteúdo
Publicidade

Mateus 8

2 Ndipo munthu wakhate anadza kwa Yesu namugwadira nati, "Ambuye, ngati mufuna, mukhoza kundiyeretsa."

3 Yesu anatambasula dzanja lake namukhudza munthuyo nati, "Ndikufuna, yeretsedwa!" Nthawi yomweyo anachiritsidwa khate lake. 4 Ndipo Yesu anati kwa iye, "Taona, usawuze wina aliyense. Koma upite kwa mkulu wa ansembe ukadzionetse wekha ndi kupereka mphatso imene Mose analamulira, kuti ukhale umboni kwa iwo."

Veja também