Publicidade

Mateus 8

26 Iye anawayankha kuti, "Inu achikhulupiriro chochepa, chifukwa chiyani mukuchita mantha?" Ndipo anayimirira nadzudzula mphepoyo ndi mafunde ndipo panali bata lalikulu.

27 Ndipo ophunzirawo anadabwa nafunsa kuti, "Ndi munthu wotani uyu? Kuti ngakhale mphepo ndi mafunde zimvera Iye!"

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-