Pular para o conteúdo
Publicidade

Mateus 9

20 Panali mayi wina amene ankadwala nthenda yotaya magazi kwa zaka khumi ndi ziwiri ndipo anadza mʼmbuyo mwake nakhudza mkanjo wake. 21 Iyeyo anati mwa iye yekha, "Nditangokhudza kasonga ka mkanjo wake, ine ndidzachiritsidwa."

22 Ndipo Yesu anatembenuka namuona mayiyo nati, "Limbani mtima mayi iwe, chikhulupiriro chako chakuchiritsa." Nthawi yomweyo mayiyo anachiritsidwa.

Veja também