Pular para o conteúdo
Publicidade

MATEYU 9

20 Panali mayi wina amene ankadwala nthenda yotaya magazi kwa zaka khumi ndi ziwiri ndipo anadza mʼmbuyo mwake nakhudza mkanjo wake. 21 Iyeyo anati mwa iye yekha, "Nditangokhudza kasonga ka mkanjo wake, ine ndidzachiritsidwa."

22 Ndipo Yesu anatembenuka namuona mayiyo nati, "Limbani mtima mayi iwe, chikhulupiriro chako chakuchiritsa." Nthawi yomweyo mayiyo anachiritsidwa.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também