3 Kudzikuza kwa mtima wako kwakusocheretsa,
iwe amene umakhala mʼmapanga a mʼmatanthwe
ndipo umamanga nyumba zako pa mapiri ataliatali,
iwe amene umanena mu mtima mwako kuti,
‘Ndani anganditsitse pansi?’
3 Kudzikuza kwa mtima wako kwakusocheretsa,
iwe amene umakhala mʼmapanga a mʼmatanthwe
ndipo umamanga nyumba zako pa mapiri ataliatali,
iwe amene umanena mu mtima mwako kuti,
‘Ndani anganditsitse pansi?’