Publicidade

Provérbios 11

1 Muyeso wachinyengo Yehova umamunyansa,

koma amakondwera ndi muyeso woyenera.

3 Ungwiro wa anthu olungama umawatsogolera,

koma anthu osakhulupirika amawonongeka ndi chinyengo chawo.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-