1 Muyeso wachinyengo Yehova umamunyansa,
koma amakondwera ndi muyeso woyenera.
3 Ungwiro wa anthu olungama umawatsogolera,
koma anthu osakhulupirika amawonongeka ndi chinyengo chawo.
1 Muyeso wachinyengo Yehova umamunyansa,
koma amakondwera ndi muyeso woyenera.
3 Ungwiro wa anthu olungama umawatsogolera,
koma anthu osakhulupirika amawonongeka ndi chinyengo chawo.