Publicidade

Provérbios 22

24 Usapalane naye ubwenzi munthu wosachedwa kupsa mtima

ndipo usayanjane ndi munthu amene sachedwa kukwiya

25 kuopa kuti iwe ungadzaphunzire njira zake

ndi kukodwa mu msampha.

Veja também

Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-07-05_19-25-13-