13 Usaleke kumulangiza mwana; ngati umulanga ndi chikwapu sadzafa. 14 Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake.
13 Usaleke kumulangiza mwana; ngati umulanga ndi chikwapu sadzafa. 14 Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake.