13 Mwana wanga, uzidya uchi popeza ndi wabwino;
uchi wochokera mʼchisa cha njuchi ndi wokoma ukawulawa.
14 Udziwe kuti nzeru ndi yoteronso pa moyo wako;
ngati uyipeza nzeruyo, zinthu zidzakuyendera bwino mʼtsogolo,
ndipo chiyembekezo chako sichidzapita pachabe.