Phindu Lina la Nzeru
1 Mwana wanga, usayiwale malangizo anga,
mtima wako usunge malamulo anga.
2 Ukatero zaka za moyo wako zidzachuluka
ndipo udzakhala pa mtendere.
1 Mwana wanga, usayiwale malangizo anga,
mtima wako usunge malamulo anga.
2 Ukatero zaka za moyo wako zidzachuluka
ndipo udzakhala pa mtendere.
+581 estão orando agora.
Junte-se à corrente de oração.