Pular para o conteúdo
Publicidade

MIYAMBO 3

11 Mwana wanga usanyoze malangizo a Yehova,

ndipo usayipidwe ndi chidzudzulo chake.

12 Paja Yehova amadzudzula amene amamukonda,

monga abambo achitira mwana amene amakondwera naye.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também