Pular para o conteúdo
Publicidade

MIYAMBO 3

3 Makhalidwe ochitira ena chifundo ndi owonetsa kukhulupirika asakuchokere.

Uwamangirire mʼkhosi mwako ngati mkanda

ndi kuwalemba pa mtima pako.

4 Ukatero udzapeza kuyanja ndi mbiri yabwino

pamaso pa Mulungu ndi anthu.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também