31 Usachite naye nsanje munthu wachiwawa
kapena kutsanzira khalidwe lake lililonse.
32 Pakuti Yehova amanyansidwa ndi munthu woyipa
koma amayanjana nawo anthu olungama.
31 Usachite naye nsanje munthu wachiwawa
kapena kutsanzira khalidwe lake lililonse.
32 Pakuti Yehova amanyansidwa ndi munthu woyipa
koma amayanjana nawo anthu olungama.