7 Usamadzione ngati wa nzeru.
Uziopa Yehova ndi kupewa zoyipa.
8 Ukatero thupi lako lidzakhala la moyo wabwino
ndi mafupa ako adzakhala olimba.
7 Usamadzione ngati wa nzeru.
Uziopa Yehova ndi kupewa zoyipa.
8 Ukatero thupi lako lidzakhala la moyo wabwino
ndi mafupa ako adzakhala olimba.