Pular para o conteúdo
Publicidade

Provérbios 31

Mathero: Mkazi Wangwiro

10 Kodi mkazi wangwiro angathe kumupeza ndani?

Ndi wokwera mtengo kuposa miyala yamtengowapatali.

11 Mtima wa mwamuna wake umamukhulupirira

ndipo mwamunayo sasowa phindu.

12 Masiku onse a moyo wake

mkaziyo amachitira mwamuna wake zabwino zokhazokha osati zoyipa.

Veja também